Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 7:5 - Buku Lopatulika

5 pakuti akonda mtundu wathu, ndipo anatimangira ife sunagoge.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 pakuti akonda mtundu wathu, ndipo anatimangira ife sunagoge.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 chifukwa amaukonda mtundu wathu, mwakuti adatimangira nyumba yamapemphero.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 chifukwa amakonda mtundu wathu ndipo anatimangira sunagoge wathu.”

Onani mutuwo Koperani




Luka 7:5
10 Mawu Ofanana  

Ndipo Hiramu mfumu ya ku Tiro anatuma anyamata ake kwa Solomoni, popeza anamva kuti adamdzoza mfumu m'malo mwa atate wake; pakuti Hiramu adakondana ndi Davide masiku onse.


Ndipo iwo, pakufika kwa Yesu, anampempha Iye koumirira, nati, Ayenera iye kuti mumchitire ichi;


Ndipo Yesu anapita nao. Ndipo pakufika Iye tsono pafupi pa nyumba yake, kenturiyo anatuma kwa Iye abwenzi ake, kunena naye, Ambuye, musadzivute; pakuti sindiyenera ine kuti mudzalowe pansi pa tsindwi langa;


Pakuti mwa Khristu Yesu kapena mdulidwe kapena kusadulidwa kulibe mphamvu; komatu chikhulupiriro, chakuchititsa mwa chikondi.


Ife tidziwa kuti tachokera kutuluka muimfa kulowa m'moyo, chifukwa tikondana ndi abale. Iye amene sakonda akhala muimfa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa