Luka 7:5 - Buku Lopatulika5 pakuti akonda mtundu wathu, ndipo anatimangira ife sunagoge. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 pakuti akonda mtundu wathu, ndipo anatimangira ife sunagoge. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 chifukwa amaukonda mtundu wathu, mwakuti adatimangira nyumba yamapemphero.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 chifukwa amakonda mtundu wathu ndipo anatimangira sunagoge wathu.” Onani mutuwo |