Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 7:49 - Buku Lopatulika

49 Ndipo iwo akuseama naye pachakudya anayamba kunena mwa okha, Uyu ndani amene akhululukiranso machimo?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

49 Ndipo iwo akuseama naye pachakudya anayamba kunena mwa okha, Uyu ndani amene akhululukiranso machimo?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

49 Apo amene ankadya naye adayamba kudzifunsa mumtima mwao kuti, “Kodi ndani uyu wokhululukira ndi machimo omweyu?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

49 Alendo enawo anayamba kumanena mʼmitima mwawo kuti, “Uyu ndi ndani amene akhululukiranso machimo?”

Onani mutuwo Koperani




Luka 7:49
4 Mawu Ofanana  

Ndipo panali pamene Iye analinkukhala pachakudya m'nyumba, onani, amisonkho ndi ochimwa ambiri anadza nakhala pansi pamodzi ndi Yesu ndi ophunzira ake.


Ndipo onani, ena a alembi ananena mumtima mwao, Uyu achitira Mulungu mwano.


Munthu amene atero bwanji? Achita mwano; akhoza ndani kukhululukira machimo, koma mmodzi, ndiye Mulungu?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa