Luka 7:48 - Buku Lopatulika48 Ndipo anati kwa mkazi, Machimo ako akhululukidwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201448 Ndipo anati kwa mkazi, Machimo ako akhululukidwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa48 Ndipo Yesu adauza mai uja kuti, “Machimo ako akhululukidwa.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero48 Kenaka anati kwa mayiyo, “Machimo ako akhululukidwa.” Onani mutuwo |