Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 7:48 - Buku Lopatulika

48 Ndipo anati kwa mkazi, Machimo ako akhululukidwa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

48 Ndipo anati kwa mkazi, Machimo ako akhululukidwa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

48 Ndipo Yesu adauza mai uja kuti, “Machimo ako akhululukidwa.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

48 Kenaka anati kwa mayiyo, “Machimo ako akhululukidwa.”

Onani mutuwo Koperani




Luka 7:48
7 Mawu Ofanana  

Ndipo onani, anabwera naye kwa Iye munthu wamanjenje, wakugona pamphasa: ndipo Yesu pakuona chikhulupiriro chao, anati kwa wodwalayo, Limba mtima, mwana, machimo ako akhululukidwa.


Pakuti chapafupi nchiti, kunena, Machimo ako akhululukidwa; kapena kunena, Tanyamuka. Nuyende?


Ndipo Yesu pakuona chikhulupiriro chao ananena ndi wodwala manjenje, Mwana, machimo ako akhululukidwa.


Chapafupi nchiti, kuuza wodwala manjenje kuti, Machimo ako akhululukidwa; kapena kuti, Nyamuka, senza mphasa yako, nuyende?


Ndipo Iye, pakuona chikhulupiriro chao, anati, Munthu iwe, machimo ako akhululukidwa.


Chapafupi nchiti, kunena, Akhululukidwa kwa iwe machimo ako; kapena kunena, Tauka, nuyende?


Chifukwa chake, ndinena kwa iwe, Machimo ake, ndiwo ambiri, akhululukidwa; chifukwa anakonda kwambiri; koma munthu amene anamkhululukira pang'ono, iye akonda pang'ono.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa