Luka 7:50 - Buku Lopatulika50 Ndipo Iye anati kwa mkaziyo, Chikhulupiriro chako chakupulumutsa iwe; muka ndi mtendere. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201450 Ndipo Iye anati kwa mkaziyo, Chikhulupiriro chako chakupulumutsa iwe; muka ndi mtendere. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa50 Koma Yesu adauza maiyo kuti, “Chikhulupiriro chanu chakupulumutsani. Pitani ndi mtendere.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero50 Yesu anati kwa mayiyo, “Chikhulupiriro chako chakupulumutsa. Pita mu mtendere.” Onani mutuwo |