Luka 7:43 - Buku Lopatulika43 Simoni anayankha, nati, Ndiyesa kuti, iye amene anamkhululukira zoposa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201443 Simoni anayankha, nati, Ndiyesa kuti, iye amene anamkhululukira zoposa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa43 Simoni adati, “Ndiyesa koma amene adamkhululukira zambiri uja.” Yesu adamuuza kuti, “Wayankha bwino.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero43 Simoni anayankha kuti, “Ndikuganiza kuti ndi amene anamukhululukira ngongole yayikulu.” Yesu anati, “Wayankha molondola.” Onani mutuwo |