Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 7:42 - Buku Lopatulika

42 Popeza analibe chobwezera iwo, anawakhululukira onse awiri. Chotero, ndani wa iwo adzaposa kumkonda?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

42 Popeza analibe chobwezera iwo, anawakhululukira onse awiri. Chotero, ndani wa iwo adzaposa kumkonda?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

42 Popeza kuti adaalibe choti abwezere, adaŵakhululukira ngongolezo onse aŵiri. Tsono iweyo ukuganiza kuti mwa aŵiriŵa ndani adzakonde wokongozayo koposa?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

42 Panalibe mmodzi mwa iwo anali ndi ndalama zobwezera, ndipo iye anawakhululukira ngongole zawo. Tsopano ndi ndani mwa awiriwa adzamukonde koposa?”

Onani mutuwo Koperani




Luka 7:42
23 Mawu Ofanana  

Ndipo mkaziyo anati, Chifukwa ninjinso munalingalira chinthu chotere pa anthu a Mulungu? Pakuti pakulankhula mau awa mfumu ikunga wopalamula, popeza mfumu siitumiza okamtenganso woingidwa wake.


Amene akhululukira mphulupulu zako zonse; nachiritsa nthenda zako zonse;


Ine, Inedi, ndine amene ndifafaniza zolakwa zako, chifukwa cha Ine mwini; ndipo Ine sindidzakumbukira machimo ako.


Ine ndafafaniza monga mtambo wochindikira zolakwa zako, ndi monga mtambo machimo ako; bwerera kwa Ine, pakuti ndakuombola.


Ndipo mbuye wa kapoloyo anagwidwa ndi chisoni mumtima, nammasula iye, namkhululukira ngongole.


Ndipo mbuye wake anakwiya, nampereka kwa azunzi, kufikira akambwezere iye mangawa onse.


Ndipo mutikhululukire mangawa athu, monga ifenso takhululukira amangawa anthu.


Simoni anayankha, nati, Ndiyesa kuti, iye amene anamkhululukira zoposa.


ndipo ayesedwa olungama kwaulere, ndi chisomo chake, mwa chiombolo cha mwa Khristu Yesu;


Pakuti pamene tinali chikhalire ofooka, pa nyengo yake Khristu anawafera osapembedza.


Pakuti onse amene atama ntchito za lamulo liwakhalira temberero; pakuti kwalembedwa, Wotembereredwa aliyense wosakhala m'zonse zolembedwa m'buku la chilamulo, kuzichita izi.


Tili ndi maomboledwe mwa mwazi wake, chikhululukiro cha zochimwa, monga mwa kulemera kwa chisomo chake,


Koma mukhalirane okoma wina ndi mnzake, a mtima wachifundo, akukhululukirana nokha, monganso Mulungu mwa Khristu anakhululukira inu.


kulolerana wina ndi mnzake, ndi kukhululukirana eni okha, ngati wina ali nacho chifukwa pa mnzake; monganso Ambuye anakhululukira inu, teroni inunso;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa