Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 7:36 - Buku Lopatulika

36 Ndipo mmodzi wa Afarisi anamuitana Iye kuti akadye naye. Ndipo analowa m'nyumba ya Mfarisi, naseama pachakudya.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

36 Ndipo mmodzi wa Afarisi anamuitana Iye kuti akadye naye. Ndipo analowa m'nyumba ya Mfarisi, naseama pachakudya.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

36 Wina wa m'gulu la Afarisi adaitana Yesu kuti akadye kwao. Yesu adapita nakaloŵa m'nyumba ya Mfarisiyo nkukakhala podyera.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

36 Tsopano mmodzi mwa Afarisi anayitana Yesu kuti akadye naye ku nyumba kwake ndipo anapita nakakhala pa tebulo.

Onani mutuwo Koperani




Luka 7:36
8 Mawu Ofanana  

Ndipo pakulankhula Iye, anamuitana Mfarisi kuti adye naye; ndipo analowa naseama kudya.


Ndipo panali pamene Iye analowa m'nyumba ya mmodzi wa akulu a Afarisi tsiku la Sabata, kukadya, iwo analikumzonda Iye.


Mwana wa Munthu wafika wakudya ndi wakumwa; ndipo munena, Onani, munthu wosusuka ndi wakumwaimwa vinyo, bwenzi la amisonkho ndi anthu ochimwa!


Ndipo nzeru iyesedwa yolungama ndi ana ake onse.


Ndipo onani, mkazi wochimwa, amene anali m'mzindamo; ndipo pakudziwa kuti Yesu analikuseama pachakudya m'nyumba ya Mfarisi, anatenga nsupa ya alabastero ya mafuta onunkhira bwino,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa