Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 7:35 - Buku Lopatulika

35 Ndipo nzeru iyesedwa yolungama ndi ana ake onse.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

35 Ndipo nzeru iyesedwa yolungama ndi ana ake onse.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

35 Komabe chilungamo cha nzeru za Mulungu chimatsimikizika ndi zochita zake.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

35 Ndipo nzeru zimaoneka zolondola mwa ana ake onse.”

Onani mutuwo Koperani




Luka 7:35
8 Mawu Ofanana  

Kodi bwanji mtengo wogulira nzeru uli m'dzanja la chitsiru, popeza wopusa alibe mtima?


Wanzeru ndani, kuti azindikire izi? Waluntha, kuti adziwe izi? Pakuti njira za Yehova zili zoongoka; ndipo olungama adzayendamo, koma olakwa adzagwamo.


Mwana wa Munthu anadza wakudya, ndi wakumwa, ndipo iwo amati, Onani munthu wakudyaidya ndi wakumwaimwa vinyo, bwenzi la amisonkho ndi ochimwa! Ndipo nzeru iyesedwa yolungama ndi ntchito zake.


Ndipo anthu onse ndi amisonkho omwe, pakumva, anavomereza kuti Mulungu ali wolungama, popeza anabatizidwa iwo ndi ubatizo wa Yohane.


Mwana wa Munthu wafika wakudya ndi wakumwa; ndipo munena, Onani, munthu wosusuka ndi wakumwaimwa vinyo, bwenzi la amisonkho ndi anthu ochimwa!


Ndipo mmodzi wa Afarisi anamuitana Iye kuti akadye naye. Ndipo analowa m'nyumba ya Mfarisi, naseama pachakudya.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa