Luka 7:37 - Buku Lopatulika37 Ndipo onani, mkazi wochimwa, amene anali m'mzindamo; ndipo pakudziwa kuti Yesu analikuseama pachakudya m'nyumba ya Mfarisi, anatenga nsupa ya alabastero ya mafuta onunkhira bwino, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201437 Ndipo onani, mkazi wochimwa, amene anali m'mudzimo; ndipo pakudziwa kuti Yesu analikuseama pachakudya m'nyumba ya Mfarisi, anatenga nsupa ya alabastero ya mafuta onunkhira bwino, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa37 M'mudzimo mudaali mai wachiwerewere. Iyeyu atamva kuti Yesu akudya m'nyumba ya Mfarisi uja, adabwera ndi nsupa yagalasi ya mafuta onunkhira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero37 Mayi amene amakhala moyo wauchimo mu mzindawo atadziwa kuti Yesu akudya ku nyumba ya Mfarisiyo, anabweretsa botolo la mafuta onunkhira a alabasta. Onani mutuwo |