Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 7:18 - Buku Lopatulika

18 Ndipo ophunzira a Yohane anamuuza iye zonsezi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

18 Ndipo ophunzira a Yohane anamuuza iye zonsezi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

18 Ophunzira a Yohane adamsimbira zonsezi Yohaneyo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

18 Ndipo ophunzira a Yohane anamuwuza Yohaneyo zinthu zonsezi. Atayitana awiri a ophunzirawo,

Onani mutuwo Koperani




Luka 7:18
3 Mawu Ofanana  

Ndipo ophunzira ake anadza, natola mtembo, nauika; ndipo anadza nauza Yesu.


Ndipo anadza kwa Yohane, nati kwa iye, Rabi, Iye amene anali ndi inu tsidya lija la Yordani, amene munamchitira umboni, taonani yemweyu abatiza, ndipo anthu onse alinkudza kwa Iye.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa