Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 7:17 - Buku Lopatulika

17 Ndipo mbiri yake imeneyo inabuka ku Yudeya yense, ndi ku dziko lonse loyandikira.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

17 Ndipo mbiri yake imeneyo inabuka ku Yudeya lonse, ndi ku dziko lonse loyandikira.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

17 Mbiri ya Yesuyi idawanda m'dziko lonse la Yudeya, ndi ku madera onse ozungulira.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

17 Mbiriyi inafalikira ku Yudeya konse ndi ku madera ozungulira.

Onani mutuwo Koperani




Luka 7:17
8 Mawu Ofanana  

Ndipo pa kubadwa kwake kwa Yesu mu Betelehemu wa Yudeya m'masiku a Herode mfumu, onani, Anzeru a kum'mawa anafika ku Yerusalemu,


Ndipo mbiri yake inabuka ku Siriya konse: ndipo anatengera kwa Iye onse akudwala, ogwidwa ndi nthenda ndi mazunzo a mitundumitundu, ndi ogwidwa ndi ziwanda, ndi akhunyu, ndi amanjenje; ndipo Iye anawachiritsa.


Ndipo mbiri yake imene inabuka m'dziko lonse limenelo.


Koma iwo anatulukamo, nabukitsa mbiri yake m'dziko lonselo.


Ndipo mbiri yake inabuka pompaja kudziko lonse la Galileya lozungulirapo.


Ndipo mfumu Herode anamva izi; pakuti dzina lake lidamveka; ndipo ananena, kuti, Yohane Mbatizi wauka kwa akufa, ndipo chifukwa chake mphamvu izi zichitachita mwa Iye.


Ndipo Yesu anabwera ndi mphamvu ya Mzimu ku Galileya; ndipo mbiri yake ya Iye inabuka ku dziko lonse loyandikira.


Ndipo anayandikira, nakhudza chithatha; ndipo akumnyamulawo anaima. Ndipo Iye anati, Mnyamata iwe, ndinena ndi iwe, Tauka.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa