Luka 7:19 - Buku Lopatulika19 Ndipo Yohane anaitana awiri a ophunzira ake, nawatuma kwa Ambuye, nanena, Kodi ndinu wakudzayo, kapena tiyang'anire wina? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Ndipo Yohane anaitana awiri a ophunzira ake, nawatuma kwa Ambuye, nanena, Kodi ndinu wakudzayo, kapena tiyang'anire wina? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Tsono iye adaitanapo ophunzira ake ena aŵiri, naŵatuma kwa Ambuye kukaŵafunsa kuti, “Kodi Inu ndinu uja ankati adzabwerayu, kapena tiziyembekezera wina?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 anawatumiza kwa Ambuye kukafunsa kuti, “Kodi ndinu anayenera kubwerayo, kapena tiyembekezere wina?” Onani mutuwo |