Luka 6:43 - Buku Lopatulika43 Pakuti palibe mtengo wabwino wakupatsa zipatso zovunda; kapenanso mtengo woipa wakupatsa zipatso zabwino. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201443 Pakuti palibe mtengo wabwino wakupatsa zipatso zovunda; kapenanso mtengo woipa wakupatsa zipatso zabwino. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa43 “Mtengo wabwino sungabale zipatso zoipa, kapenanso mtengo woipa kubala zipatso zabwino. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero43 Palibe mtengo wabwino umene umabala chipatso choyipa, kapena mtengo oyipa umene umabala chipatso chabwino. Onani mutuwo |