Luka 6:30 - Buku Lopatulika30 Munthu aliyense akakupempha kanthu, umpatse; ndi iye amene alanda zako, usazipemphanso. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201430 Munthu aliyense akakupempha kanthu, umpatse; ndi iye amene alanda zako, usazipemphanso. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa30 Munthu akakupempha kanthu, uzimpatsa. Ndipo munthu akatenga zinthu zako, usamlamule kuti abweze. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero30 Mupatseni aliyense amene akupemphani kanthu ndipo ngati wina atenga chinthu chanu, musamulamule kuti akubwezereni. Onani mutuwo |