Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Luka 6:31 - Buku Lopatulika

31 Ndipo monga mufuna inu kuti anthu adzakuchitirani inu, muwachitire iwo motero inu momwe.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

31 Ndipo monga mufuna inu kuti anthu adzakuchitirani inu, muwachitire iwo motero inu momwe.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

31 Zomwe mukufuna kuti anthu akuchitireni, inuyo muŵachitire zomwezo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

31 Inu muwachitire anthu ena, zomwe mukanafuna kuti iwo akuchitireni.

Onani mutuwo Koperani




Luka 6:31
5 Mawu Ofanana  

Ndipo lachiwiri lolingana nalo ndili, Uzikonda mnzako monga udzikonda iwe mwini.


Chifukwa chake zinthu zilizonse mukafuna kuti anthu achitire inu, inunso muwachitire iwo zotero; pakuti icho ndicho chilamulo ndi aneneri.


Munthu aliyense akakupempha kanthu, umpatse; ndi iye amene alanda zako, usazipemphanso.


Pakuti mau amodzi akwaniritsa chilamulo chonse ndiwo; Uzikonda mnzako monga udzikonda iwe mwini.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa