Luka 6:31 - Buku Lopatulika31 Ndipo monga mufuna inu kuti anthu adzakuchitirani inu, muwachitire iwo motero inu momwe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201431 Ndipo monga mufuna inu kuti anthu adzakuchitirani inu, muwachitire iwo motero inu momwe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa31 Zomwe mukufuna kuti anthu akuchitireni, inuyo muŵachitire zomwezo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero31 Inu muwachitire anthu ena, zomwe mukanafuna kuti iwo akuchitireni. Onani mutuwo |