Luka 6:20 - Buku Lopatulika20 Ndipo Iye anakweza maso ake kwa ophunzira ake, nanena, Odala osauka inu; chifukwa uli wanu ufumu wa Mulungu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Ndipo Iye anakweza maso ake kwa ophunzira ake, nanena, Odala osauka inu; chifukwa uli wanu ufumu wa Mulungu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Yesu adayang'ana ophunzira ake, naŵauza kuti, “Ndinu odala, inu osaukanu, Ufumu wa Mulungu ndi wanu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Akuyangʼana ophunzira ake, Iye anati, “Odala ndinu amene ndi osauka, chifukwa ufumu wa Mulungu ndi wanu. Onani mutuwo |