Luka 6:19 - Buku Lopatulika19 ndi khamu lonse lija linafuna kumkhudza Iye; chifukwa munatuluka mphamvu mwa Iye, nkuchiritsa onsewa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 ndi khamu lonse lija linafuna kumkhudza Iye; chifukwa munatuluka mphamvu mwa Iye, nichiritsa onsewa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Anthu onsewo ankafuna kumkhudza, chifukwa mphamvu zinkatuluka mwa Iye ndi kuŵachiritsa onse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 ndipo anthu ankayesetsa kuti amukhudze chifukwa mphamvu imatuluka mwa Iye ndi kuchiritsa onse. Onani mutuwo |