Luka 6:18 - Buku Lopatulika18 ndipo ovutidwa ndi mizimu yonyansa anachiritsidwa, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 ndipo ovutidwa ndi mizimu yonyansa anachiritsidwa, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Iwo adabwera kudzamva mau ake, ndiponso kuti Iye aŵachiritse. Anthu amene ankasautsidwa ndi mizimu yoipa, amenewonso Iye ankaŵachiritsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Iwo anabwera kudzamvetsera ndi kuchiritsidwa ku matenda awo. Osautsidwa ndi mizimu yoyipa anachiritsidwa, Onani mutuwo |