Luka 6:21 - Buku Lopatulika21 Odala inu akumva njala tsopano; chifukwa mudzakhuta. Odala inu akulira tsopano; chifukwa mudzaseka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Odala inu akumva njala tsopano; chifukwa mudzakhuta. Odala inu akulira tsopano; chifukwa mudzaseka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 “Ndinu odala, inu amene mukumva njala tsopano, chifukwa mudzakhuta. “Ndinu odala, inu amene mukulira tsopano, chifukwa mudzakondwa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Inu amene mukumva njala tsopano, ndinu odala chifukwa mudzakhutitsidwa. Inu amene mukulira tsopano, ndinu odala chifukwa mudzasekerera. Onani mutuwo |