Luka 5:29 - Buku Lopatulika29 Ndipo Levi anamkonzera Iye phwando lalikulu kunyumba kwake; ndipo panali khamu lalikulu la amisonkho, ndi enanso amene analikuseama pachakudya pamodzi nao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201429 Ndipo Levi anamkonzera Iye phwando lalikulu kunyumba kwake; ndipo panali khamu lalikulu la amisonkho, ndi enanso amene analikuseama pachakudya pamodzi nao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa29 Tsono Levi adamkonzera Yesu phwando lalikulu kunyumba kwake. Okhometsa msonkho ambirimbiri, pamodzi ndi anthu ena, anali nao paphwandopo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero29 Kenaka Levi anakonzera Yesu phwando lalikulu ku nyumba yake ndipo gulu lalikulu la amisonkho ndi ena ankadya naye pamodzi. Onani mutuwo |