Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 5:27 - Buku Lopatulika

27 Ndipo zitatha izi Iye anatuluka, naona munthu wamsonkho, dzina lake Levi, alikukhala polandirira msonkho, nati kwa iye, Unditsate Ine.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

27 Ndipo zitatha izi Iye anatuluka, naona munthu wamsonkho, dzina lake Levi, alikukhala polandirira msonkho, nati kwa iye, Unditsate Ine.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

27 Pambuyo pake Yesu adatuluka naona munthu wokhometsa msonkho, dzina lake Levi, ali pa ntchito m'nyumba ya msonkho. Adamuuza kuti, “Iwe, unditsate.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

27 Zitatha izi, Yesu anachoka ndipo anaona wolandira msonkho dzina lake Levi atakhala mʼnyumba ya msonkho. Yesu anati kwa iye, “Nditsate Ine.”

Onani mutuwo Koperani




Luka 5:27
11 Mawu Ofanana  

Filipo, ndi Bartolomeo; Tomasi, ndi Mateyu wamsonkho yo; Yakobo mwana wa Alifeyo, ndi Tadeyo;


Pomwepo Yesu anati kwa ophunzira ake, Ngati munthu afuna kudza pambuyo panga, adzikane yekha, natenge mtanda wake, nanditsate Ine.


Koma Yesu ananena kwa iye, Tsata Ine, nuleke akufa aike akufa ao.


ndi Andrea, ndi Filipo, ndi Bartolomeo, ndi Mateyu, ndi Tomasi, ndi Yakobo mwana wa Alifeyo, ndi Tadeyo, ndi Simoni Mkanani,


Koma m'mene Yesu anamva, anati kwa iye, Usowa chinthu chimodzi: gulitsa zilizonse uli nazo, nugawire osauka; ndipo udzakhala nacho chuma chenicheni mu Mwamba; ndipo ukadze kuno, unditsate Ine.


M'mawa mwake anafuna kutuluka kunka ku Galileya, napeza Filipo. Ndipo Yesu ananena naye, Tsata Ine.


Ngati wina anditumikira Ine, anditsate; ndipo kumene kuli Ine, komwekonso kudzakhala mtumiki wanga. Ngati wina anditumikira Ine, Atate adzamchitira ulemu iyeyu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa