Luka 5:25 - Buku Lopatulika25 Ndipo pomwepo anaimirira pamaso pao, nasenza chimene adagonapo, nachokapo, kunka kunyumba kwake, wakulemekeza Mulungu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201425 Ndipo pomwepo anaimirira pamaso pao, nasenza chimene adagonapo, nachokapo, kunka kunyumba kwake, wakulemekeza Mulungu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa25 Pomwepo wodwalayo adadzukadi onse akupenya, ndipo adatenga machira aja amene adaagonapo, namapita kwao akutamanda Mulungu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero25 Nthawi yomweyo anayimirira patsogolo pawo, nanyamula mphasa yake ndipo anapita kwawo akuyamika Mulungu. Onani mutuwo |