Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 4:44 - Buku Lopatulika

44 Ndipo Iye analikulalikira m'masunagoge a ku Yudeya.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

44 Ndipo Iye analikulalikira m'masunagoge a ku Yudeya.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

44 Motero Iye ankalalika m'nyumba zamapemphero za ku Yudeya.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

44 Ndipo Iye anapitirirabe kulalikira mʼmasunagoge a ku Yudeya.

Onani mutuwo Koperani




Luka 4:44
4 Mawu Ofanana  

Ndipo Yesu anayendayenda mu Galileya monse, analikuphunzitsa m'masunagoge mwao, nalalikira Uthenga Wabwino wa Ufumu, nachiritsa nthenda zonse ndi kudwala konse mwa anthu.


Ndipo analowa m'masunagoge mwao mu Galileya monse, nalalikira, natulutsa ziwanda.


Ndipo Iye anaphunzitsa m'masunagoge mwao, nalemekezedwa ndi anthu onse.


Ndipo panali, pakumkanikiza khamu la anthu, kudzamva mau a Mulungu, Iye analikuimirira m'mbali mwa nyanja ya Genesarete;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa