Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 4:21 - Buku Lopatulika

21 Ndipo anayamba kunena kwa iwo, kuti, Lero lembo ili lakwanitsidwa m'makutu anu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

21 Ndipo anayamba kunena kwa iwo, kuti, Lero lembo ili lakwanitsidwa m'makutu anu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

21 Tsono Yesu adaŵauza kuti, “Lero zachitikadi zimene adaaneneratu Malembo amene mwamvaŵa.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

21 ndipo anawawuza kuti, “Lero malemba awa akwaniritsidwa mmene mwamveramu.”

Onani mutuwo Koperani




Luka 4:21
9 Mawu Ofanana  

Ndipo adzachitidwa kwa iwo mau adanenera Yesaya, amene ati, Pakumva mudzamva, ndipo simudzazindikira konse; pakupenya mudzapenya, ndipo simudzaona konse.


Ndipo m'mene Iye anapinda bukulo, nalipereka kwa mnyamata, anakhala pansi; ndipo maso ao a anthu onse m'sunagogemo anamyang'anitsa Iye.


Ndipo onse anamchitira Iye umboni nazizwa ndi mau a chisomo akutuluka m'kamwa mwake; nanena, Kodi uyu si mwana wa Yosefe?


Musanthula m'malembo, popeza muyesa kuti momwemo muli nao moyo wosatha; ndipo akundichitira Ine umboni ndi iwo omwewo;


Koma zimene Mulungu analalikiratu m'kamwa mwa aneneri onse, kuti adzamva kuwawa Khristu, Iye anakwaniritsa chotero.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa