Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 24:34 - Buku Lopatulika

34 nanena, Ambuye anauka ndithu, naonekera kwa Simoni.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

34 nanena, Ambuye anauka ndithu, naonekera kwa Simoni.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

34 akunena kuti, “Ambuye adaukadi, ndipo Simoni waŵaona.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

34 ndipo anati, “Ndi zoonadi! Ambuye auka ndipo anaonekera kwa Simoni.”

Onani mutuwo Koperani




Luka 24:34
7 Mawu Ofanana  

Koma mukani, uzani ophunzira ake, ndi Petro, kuti akutsogolerani inu ku Galileya; kumeneko mudzamuona Iye, monga ananena ndi inu.


Palibe kuno Iye, komatu anauka; kumbukirani muja adalankhula nanu, pamene analinso mu Galileya,


Ndipo pamene Ambuye anamuona, anagwidwa ndi chifundo chifukwa cha iye, nanena naye, Usalire.


Ndipo Yohane anaitana awiri a ophunzira ake, nawatuma kwa Ambuye, nanena, Kodi ndinu wakudzayo, kapena tiyang'anire wina?


kwa iwonso anadzionetsera yekha wamoyo ndi zitsimikizo zambiri, zitatha zowawa zake, naonekera kwa iwo masiku makumi anai, ndi kunena zinthu za Ufumu wa Mulungu;


ndi kuti anaonekera kwa Kefa; pamenepo kwa khumi ndi awiriwo;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa