Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Luka 24:33 - Buku Lopatulika

33 Ndipo ananyamuka nthawi yomweyo nabwera ku Yerusalemu, napeza khumi ndi mmodziwo, ndi iwo anali nao atasonkhana pamodzi,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

33 Ndipo ananyamuka nthawi yomweyo nabwera ku Yerusalemu, napeza khumi ndi mmodziwo, ndi iwo anali nao atasonkhana pamodzi,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

33 Nthaŵi yomweyo adanyamuka kubwerera ku Yerusalemu. Adakapeza ophunzira khumi ndi mmodzi aja atasonkhana pamodzi ndi anzao ena,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

33 Nthawi yomweyo iwo anayimirira ndi kubwerera ku Yerusalemu. Iwo anapeza khumi ndi mmodziwo ndi ena anali nawo nasonkhana pamodzi

Onani mutuwo Koperani




Luka 24:33
4 Mawu Ofanana  

Ndipo iwowa anachoka nawauza otsala; koma iwo omwe sanawavomereze.


Iwo onse analikukangalika m'kupemphera, pamodzi ndi akazi, ndi Maria, amake wa Yesu, ndi abale ake omwe.


pomwepo anaonekera kwa Yakobo; pamenepo kwa atumwi onse;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa