Luka 24:25 - Buku Lopatulika25 Ndipo Iye anati kwa iwo, Opusa inu, ndi ozengereza mtima kusakhulupirira zonse adazilankhula aneneri! Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201425 Ndipo Iye anati kwa iwo, Opusa inu, ndi ozengereza mtima kusakhulupirira zonse adazilankhula aneneri! Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa25 Apo Yesu adati, “Ha! Koma ndiye ndinu anthu opusa, osafuna kukhulupirira msanga zonse zija zimene aneneri adanena. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero25 Iye anawawuza kuti, “Inu ndinu anthu opusa, osafuna kukhulupirira msanga zonse zimene aneneri ananena! Onani mutuwo |