Luka 24:26 - Buku Lopatulika26 Kodi sanayenere Khristu kumva zowawa izi, ndi kulowa ulemerero wake? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 Kodi sanayenera Khristu kumva zowawa izi, ndi kulowa ulemerero wake? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 Kodi inu simukudziŵa kuti Mpulumutsi wolonjezedwa uja adaayenera kumva zoŵaŵa zonsezi kuti aloŵe mu ulemerero wake?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 Kodi Khristu sanayenera kumva zowawa izi ndipo kenaka ndi kulowa mu ulemerero wake?” Onani mutuwo |
Ndipo atapita masabata makumi asanu ndi limodzi mphambu awiri wodzozedwayo adzalikhidwa, nadzakhala wopanda kanthu; ndi anthu a kalonga wakudzayo adzaononga mzinda ndi malo opatulika; ndi kutsiriza kwake kudzakhala kwa chigumula, ndi kufikira chimaliziro kudzakhala nkhondo; chipasuko chalembedweratu.