Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 23:53 - Buku Lopatulika

53 Ndipo anautsitsa, naukulunga m'nsalu yabafuta, nauika m'manda osemedwa m'mwala, m'menemo sanaike munthu ndi kale lonse.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

53 Ndipo anautsitsa, naukulunga m'nsalu yabafuta, nauika m'manda osemedwa m'mwala, m'menemo sanaike munthu ndi kale lonse.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

53 Tsono adautsitsa naukulunga m'nsalu yoyera yabafuta, nkuuika m'manda. Mandawo anali asanaikemo munthu wina aliyense.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

53 Ndipo anawutsitsa, nawukulunga nsalu yabafuta nawuyika mʼmanda wosemedwa mʼmwala, amene panalibe wina amene anayikidwamo.

Onani mutuwo Koperani




Luka 23:53
7 Mawu Ofanana  

Ndipo anaika manda ake pamodzi ndi oipa, ndi pamodzi ndi olemera mu imfa yake, ngakhale Iye sanachite chiwawa, ndipo m'kamwa mwake munalibe chinyengo.


Ndipo anagula bafuta, namtsitsa Iye, namkulunga m'bafutamo, namuika m'manda osemedwa m'thanthwe; nakunkhunizira mwala pakhomo la manda.


yemweyo anapita kwa Pilato napempha mtembo wake wa Yesu.


Ndipo panali tsiku lokonzera, ndi Sabata linayandikira.


Koma kunali munda kumalo kumene anapachikidwako, ndi m'mundamo munali manda atsopano m'mene sanaikidwemo munthu aliyense nthawi zonse.


Ndipo atatsiriza zonse zolembedwa za Iye, anamtsitsa kumtengo, namuika m'manda.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa