Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 23:54 - Buku Lopatulika

54 Ndipo panali tsiku lokonzera, ndi Sabata linayandikira.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

54 Ndipo panali tsiku lokonzera, ndi Sabata linayandikira.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

54 Linali tsiku la chikonzero, tsiku la Sabata likuti liziyamba kumene.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

54 Linali tsiku lokonzekera ndipo Sabata linatsala pangʼono kuyamba.

Onani mutuwo Koperani




Luka 23:54
6 Mawu Ofanana  

Ndipo m'mawa mwake, ndilo tsiku lotsatana ndi tsiku lokonzera, ansembe aakulu ndi Afarisi anasonkhana kwa Pilato,


Ndipo atafika tsono madzulo, popeza mpa tsiku lokonzekera, ndilo la pambuyo pa Sabata,


Ndipo anautsitsa, naukulunga m'nsalu yabafuta, nauika m'manda osemedwa m'mwala, m'menemo sanaike munthu ndi kale lonse.


Koma linali tsiku lokonza Paska; panali monga ora lachisanu ndi chimodzi. Ndipo ananena kwa Ayuda, Taonani, mfumu yanu!


Pomwepo Ayuda, popeza panali tsiku lokonzera, kuti mitembo ingatsale pamtanda tsiku la Sabata, pakuti tsiku lomwelo la Sabata linali lalikulu, anapempha Pilato kuti miyendo yao ithyoledwe, ndipo achotsedwe.


Pomwepo ndipo anaika Yesu, chifukwa cha tsiku lokonzera la Ayuda, pakuti mandawo anali pafupi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa