Luka 23:41 - Buku Lopatulika41 Ndipo ifetu kuyenera; pakuti tilikulandira zoyenera zimene tinazichita: koma munthu uyu sanachite kanthu kolakwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201441 Ndipo ifetu kuyenera; pakuti tilikulandira zoyenera zimene tinazichita: koma munthu uyu sanachite kanthu kolakwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa41 Tsonotu ife zikutiyeneradi zimenezi, tikulandira zolingana ndi zimene tidachita. Koma aŵa sadachite cholakwa chilichonse.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero41 Ife tikulangidwa mwachilungamo, pakuti ife tikulandira monga mwa ntchito zathu. Koma munthu uyu sanachimwe kanthu.” Onani mutuwo |