Luka 23:40 - Buku Lopatulika40 Koma winayo anayankha, namdzudzula iye, nati, Kodi suopa Mulungu, poona uli m'kulangika komweku? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201440 Koma winayo anayankha, namdzudzula iye, nati, Kodi suopa Mulungu, poona uli m'kulangika komweku? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa40 Koma mnzake uja adamdzudzula, adati, “Kodi iwe, suwopa ndi Mulungu yemwe, chidziŵirecho kuti nawenso ukulandira chilango chomwechi? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero40 Koma wachifwamba winayo anamudzudzula iye nati, “Suopa Mulungu, iwenso ukulandira chilango chomwechi? Onani mutuwo |