Luka 23:42 - Buku Lopatulika42 Ndipo ananena, Yesu, ndikumbukireni m'mene mulowa Ufumu wanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201442 Ndipo ananena, Yesu, ndikumbukireni m'mene mulowa Ufumu wanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa42 Ndipo adati, “Inu, mukandikumbikire mukakafika mu Ufumu wanu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero42 Kenaka anati, “Yesu, mundikumbukire ine pamene mulowa mu ufumu wanu.” Onani mutuwo |