Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Luka 23:42 - Buku Lopatulika

42 Ndipo ananena, Yesu, ndikumbukireni m'mene mulowa Ufumu wanu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

42 Ndipo ananena, Yesu, ndikumbukireni m'mene mulowa Ufumu wanu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

42 Ndipo adati, “Inu, mukandikumbikire mukakafika mu Ufumu wanu.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

42 Kenaka anati, “Yesu, mundikumbukire ine pamene mulowa mu ufumu wanu.”

Onani mutuwo Koperani




Luka 23:42
20 Mawu Ofanana  

Koma Ine ndadzoza mfumu yanga Pa Ziyoni, phiri langa loyera.


Ndipo ndinena kwa inu, Amene aliyense akavomereza Ine pamaso pa anthu, inde, Mwana wa Munthu adzamvomereza iye pamaso pa angelo a Mulungu;


Koma wamsonkhoyo alikuima patali sanafune kungakhale kukweza maso kumwamba, komatu anadziguguda pachifuwa pake nanena, Mulungu, mundichitire chifundo, ine wochimwa.


Ndipo ifetu kuyenera; pakuti tilikulandira zoyenera zimene tinazichita: koma munthu uyu sanachite kanthu kolakwa.


Ndipo Iye ananena naye, Indetu, ndinena ndi iwe, Lero lino udzakhala ndine mu Paradaiso.


Kodi sanayenere Khristu kumva zowawa izi, ndi kulowa ulemerero wake?


Natanaele anayankha Iye, Rabi, Inu ndinu Mwana wa Mulungu, ndinu mfumu ya Israele.


Tomasi anayankha nati kwa Iye, Ambuye wanga, ndi Mulungu wanga.


Ndipo iwo anati, Ukhulupirire Ambuye Yesu, ndipo udzapulumuka, iwe ndi apabanja ako.


ndi kuchitira umboni Ayuda ndi Agriki wa kutembenuka mtima kulinga kwa Mulungu, ndi chikhulupiriro cholinga kwa Ambuye wathu Yesu Khristu.


ndi kusanthula nthawi yiti, kapena nthawi yanji Mzimu wa Khristu wokhala mwa iwo analozera, pakuchitiratu umboni wa masautso a Khristu, ndi ulemerero wotsatana nao.


Yense wokhulupirira kuti Yesu ndiye Khristu wabadwa kuchokera kwa Mulungu; ndipo yense wakukonda Iye amene anabala akondanso iye amene anabadwa wochokera mwa Iye.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa