Luka 23:3 - Buku Lopatulika3 Ndipo Pilato anamfunsa Iye, nanena, Kodi ndiwe mfumu ya Ayuda? Ndipo Iye anamyankha nati, Mwatero. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndipo Pilato anamfunsa Iye, nanena, Kodi ndiwe mfumu ya Ayuda? Ndipo Iye anamyankha nati, Mwatero. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Pilato adafunsa Yesu kuti, “Kodi iwe, ndiwe Mfumu ya Ayuda?” Yesu adati, “Mwanena nokha.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Pamenepo Pilato anamufunsa Yesu kuti, “Kodi Iwe ndiwe Mfumu ya Ayuda?” Yesu anayankha kuti, “Mwatero ndinu.” Onani mutuwo |