Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 23:23 - Buku Lopatulika

23 Koma anakakamiza ndi mau okweza, napempha kuti Iye apachikidwe. Ndipo mau ao anapambana.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

23 Koma anakakamiza ndi mau okweza, napempha kuti Iye apachikidwe. Ndipo mau ao analakika.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

23 Koma iwo adamuumiriza mokweza mau kuti Yesu apachikidwe, kufuula kwao kunkakulirakulira.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

23 Koma ndi mawu ofuwulitsa, analimbikirabe kuti Iye apachikidwe, ndipo kufuwulako kunapitirira.

Onani mutuwo Koperani




Luka 23:23
7 Mawu Ofanana  

Moyo wanga uli pakati pa mikango; ndigona pakati pa oyaka moto, ndiwo ana a anthu amene mano ao ali nthungo ndi mivi, ndipo lilime lao ndilo lupanga lakuthwa.


Ndipo ndinatha abusa atatuwo mwezi umodzi; pakuti mtima wanga unalema nao, ndi mtima waonso unaipidwa nane.


Koma iye analimbitsa mau chilimbitsire, kuti, Ngakhale ndidzafa nanu, sindidzakana Inu. Ndipo onsewo anatero.


Ndipo anati kwa iwo nthawi yachitatu, Nanga munthuyu anachita choipa chiyani? Sindinapeze chifukwa cha kufera Iye; chotero ndidzamkwapula Iye ndi kummasula.


Ndipo Pilato anaweruza kuti chimene alikufunsa chichitidwe.


Koma iwo anapunda kunena kuti, Amautsa anthuwo, naphunzitsa mu Yudeya yense, kuyambira ku Galileya ndi kufikira kuno komwe.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa