Luka 23:22 - Buku Lopatulika22 Ndipo anati kwa iwo nthawi yachitatu, Nanga munthuyu anachita choipa chiyani? Sindinapeze chifukwa cha kufera Iye; chotero ndidzamkwapula Iye ndi kummasula. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Ndipo anati kwa iwo nthawi yachitatu, Nanga munthuyu anachita choipa chiyani? Sindinapeza chifukwa cha kufera Iye; chotero ndidzamkwapula Iye ndi kummasula. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Pilato adaŵafunsa kachitatu kuti, “Koma wachimwanji Iyeyu? Sindikumpeza mlandu woyenera kumuphera. Motero ndingomukwapula kenaka ndimmasula.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Kachitatu anawafunsanso iwo kuti, “Chifukwa chiyani? Kodi munthu uyu wachita choyipa chanji? Ine sindinapeze cholakwa mwa Iye chakuti aphedwe choncho ndingomukwapula ndi kumumasula.” Onani mutuwo |