Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Luka 23:24 - Buku Lopatulika

24 Ndipo Pilato anaweruza kuti chimene alikufunsa chichitidwe.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

24 Ndipo Pilato anaweruza kuti chimene alikufunsa chichitidwe.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

24 Tsono Pilato adagamula kuti zimene anthu aja ankapempha zichitike.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

24 Choncho Pilato anatsimikiza kuchita zofuna zawozo.

Onani mutuwo Koperani




Luka 23:24
7 Mawu Ofanana  

Usatsata unyinji wa anthu kuchita choipa; kapena usachita umboni kumlandu, ndi kupatukira kutsata unyinji ndi kukhotetsa mlandu;


Wokometsa mlandu wa wamphulupulu, ndi wotsutsa wolungama, onse awiriwa amnyansa Yehova.


Pomwepo iye anamasulira iwo Barabasi, koma anakwapula Yesu, nampereka Iye kuti akampachike pamtanda.


Ndipo Pilato pofuna kuwakhazika mtima anthuwo, anawamasulira Barabasi, napereka Yesu, atamkwapula, akampachike pamtanda.


Koma anakakamiza ndi mau okweza, napempha kuti Iye apachikidwe. Ndipo mau ao anapambana.


Ndipo anawamasulira amene adaponyedwa m'ndende chifukwa cha mpanduko ndi kupha munthu, amene iwo anampempha; koma anapereka Yesu mwa chifuniro chao.


Pamenepo tsono Pilato anatenga Yesu, namkwapula.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa