Luka 23:18 - Buku Lopatulika18 Koma iwo onse pamodzi anafuula, nati, Chotsani munthu uyu, mutimasulire Barabasi; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Koma iwo onse pamodzi anafuula, nati, Chotsani munthu uyu, mutimasulire Barabasi; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Koma anthu onse aja adayamba kufuula pamodzi kuti, “Mchotseni ameneyu, mutimasulire Barabasi.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Onse pamodzi anafuwula kuti, “Muchotseni munthuyu! Timasulireni Baraba!” Onani mutuwo |