Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 23:16 - Buku Lopatulika

16 Chifukwa chake ndidzamkwapula ndi kummasula Iye.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

16 Chifukwa chake ndidzamkwapula ndi kummasula Iye.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

16 Motero ndingomukwapula kenaka nkumumasula.” [

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

16 Nʼchifukwa chake, ine ndingomulanga, nʼkumumasula.”

Onani mutuwo Koperani




Luka 23:16
9 Mawu Ofanana  

Koma Iye analasidwa chifukwa cha zolakwa zathu, natundudzidwa chifukwa cha mphulupulu zathu; chilango chotitengera ife mtendere chinamgwera Iye; ndipo ndi mikwingwirima yake ife tachiritsidwa.


Pomwepo iye anamasulira iwo Barabasi, koma anakwapula Yesu, nampereka Iye kuti akampachike pamtanda.


Ndipo Pilato pofuna kuwakhazika mtima anthuwo, anawamasulira Barabasi, napereka Yesu, atamkwapula, akampachike pamtanda.


Ndipo anati kwa iwo nthawi yachitatu, Nanga munthuyu anachita choipa chiyani? Sindinapeze chifukwa cha kufera Iye; chotero ndidzamkwapula Iye ndi kummasula.


Ndipo musawatsutsa, ndipo simudzamatsutsidwa. Khululukani, ndipo mudzakhululukidwa.


Koma Paulo anati kwa iwo, Adatikwapula ife pamaso pa anthu, osamva mlandu wathu, ife amene tili Aroma, natiika m'ndende; ndipo tsopano kodi afuna kutitulutsira ife m'tseri? Iai, ndithu; koma adze okha atitulutse.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa