Luka 23:19 - Buku Lopatulika19 ndiye munthu anaponyedwa m'ndende chifukwa cha mpanduko m'mzinda ndi cha kupha munthu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 ndiye munthu anaponyedwa m'ndende chifukwa cha mpanduko m'mudzi ndi cha kupha munthu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Barabasi anali atamponya m'ndende chifukwa cha kuyambitsa chipolowe mu mzinda, ndiponso kupha munthu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 (Baraba anaponyedwa mʼndende chifukwa choyambitsa chipolowe mu mzinda ndi kupha). Onani mutuwo |