Luka 23:1 - Buku Lopatulika1 Ndipo khamu lonselo linanyamuka kupita naye kwa Pilato. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipo khamu lonselo linanyamuka kupita naye kwa Pilato. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Gulu lonse lija lidanyamuka nkupita naye Yesu kwa Pilato. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Kenaka gulu lonse la anthuwo linayimirira ndi kumutengera kwa Pilato. Onani mutuwo |