Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 23:1 - Buku Lopatulika

1 Ndipo khamu lonselo linanyamuka kupita naye kwa Pilato.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Ndipo khamu lonselo linanyamuka kupita naye kwa Pilato.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 Gulu lonse lija lidanyamuka nkupita naye Yesu kwa Pilato.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Kenaka gulu lonse la anthuwo linayimirira ndi kumutengera kwa Pilato.

Onani mutuwo Koperani




Luka 23:1
7 Mawu Ofanana  

Ndipo pamene kunacha, bungwe la akulu a anthu linasonkhana, ndiwo ansembe aakulu ndi alembi; ndipo anapita naye kubwalo lao,


Ndipo iwo anati, Tifuniranjinso mboni? Pakuti ife tokha tinamva m'kamwa mwa Iye mwini.


Pakuti zoonadi anasonkhanidwa m'mzinda muno Herode, ndi Pontio Pilato yemwe pamodzi ndi amitundu ndi anthu a Israele kumchitira choipa Mwana wanu wopatulika Yesu amene munamdzoza;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa