Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 22:71 - Buku Lopatulika

71 Ndipo iwo anati, Tifuniranjinso mboni? Pakuti ife tokha tinamva m'kamwa mwa Iye mwini.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

71 Ndipo iwo anati, Tifuniranjinso mboni? Pakuti ife tokha tinamva m'kamwa mwa Iye mwini.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

71 Pamenepo iwo aja adati, “Tikufuniranji umboni wina? Tadzimvera tokha mau akeŵa.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

71 Pamenepo iwo anati, “Nanga tikufuniranjinso umboni wina? Ife tamva kuchokera pa milomo yake.”

Onani mutuwo Koperani




Luka 22:71
4 Mawu Ofanana  

Ndipo onse anati, Umo mtero, muli Mwana wa Mulungu kodi? Ndipo Iye anati kwa iwo, Munena kuti ndine.


Ndipo khamu lonselo linanyamuka kupita naye kwa Pilato.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa