Luka 22:70 - Buku Lopatulika70 Ndipo onse anati, Umo mtero, muli Mwana wa Mulungu kodi? Ndipo Iye anati kwa iwo, Munena kuti ndine. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201470 Ndipo onse anati, Umo mtero, muli Mwana wa Mulungu kodi? Ndipo Iye anati kwa iwo, Munena kuti ndine. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa70 Apo onse aja adati, “Tsono ndiye kutitu ndiwe Mwana wa Mulungu, ati?” Yesu adati, “Mwanena nokha kuti ndine amene.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero70 Onse anafunsa kuti, “Ndiye kuti ndiwe Mwana wa Mulungu?” Iye anayankha kuti, “Mwanena ndinu kuti Ndine.” Onani mutuwo |