Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 22:9 - Buku Lopatulika

9 Ndipo iwo ananena naye, Mufuna tikakonzere kuti?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Ndipo iwo ananena naye, Mufuna tikakonzere kuti?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Koma iwo adamufunsa kuti, “Kodi tikakonzere kuti?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Iwo anafunsa kuti, “Kodi mukufuna tikakonzere kuti?”

Onani mutuwo Koperani




Luka 22:9
3 Mawu Ofanana  

Ndipo Iye anayamba kulankhula nao m'mafanizo. Munthu analima munda wampesa, nauzunguniza ndi linga, nakumba moponderamo mphesa, namanga nsanja, naukongoletsa kwa olima munda, namuka kwina.


Ndipo Iye anati kwa iwo, Onani, mutalowa m'mzinda, adzakomana ndinu munthu alikusenza mtsuko wa madzi; mumtsate ameneyo kunyumba kumene akalowako iye.


Ndipo Iye anatumiza Petro ndi Yohane, nati, Pitani mutikonzere ife Paska, kuti tidye.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa