Luka 22:60 - Buku Lopatulika60 Koma Petro anati, Munthu iwe, sindidziwa chimene uchinena. Ndipo pomwepo, iye ali chilankhulire, tambala analira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201460 Koma Petro anati, Munthu iwe, sindidziwa chimene uchinena. Ndipo pomwepo, iye ali chilankhulire, tambala analira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa60 Koma Petro adati, “Munthu iwe, sindikuzidziŵa zimene ukunenazi.” Ndipo pompo, akulankhulabe, tambala adalira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero60 Petro anayankha kuti, “Munthu iwe, sindikudziwa zimene ukunena apa.” Pamene iye ankayankhula, tambala analira. Onani mutuwo |