Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Luka 22:59 - Buku Lopatulika

59 Ndipo patapita ngati ora limodzi, wina ananenetsa, kuti, Zoonadi, munthu uyunso anali naye, pakuti ndiye Mgalileya

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

59 Ndipo patapita ngati ora limodzi, wina ananenetsa, kuti, Zoonadi, munthu uyunso anali naye, pakuti ndiye Mgalileya

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

59 Patapita ngati ora limodzi, munthu winanso adanenetsa kuti, “Ndithudi akulu aŵanso anali naye, pakuti ndi a ku Galileya.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

59 Patatha pafupifupi ora limodzi, munthu winanso anati, “Zoonadi, munthu uyu anali ndi Iye, pakuti ndi mu Galileya.”

Onani mutuwo Koperani




Luka 22:59
5 Mawu Ofanana  

Koma Petro anati, Munthu iwe, sindidziwa chimene uchinena. Ndipo pomwepo, iye ali chilankhulire, tambala analira.


Koma anati kwa iye, Wamisala iwe. Ndipo analimbika ndi kunena kuti nkutero. Ndipo ananena, Ndiye mngelo wake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa