Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 22:6 - Buku Lopatulika

6 Ndipo iye anavomera, nafunafuna nthawi yabwino yakumpereka Iye kwa iwo, pakalibe khamu la anthu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 Ndipo iye anavomera, nafunafuna nthawi yabwino yakumpereka Iye kwa iwo, pakalibe khamu la anthu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 Yudasi adavomera, nayamba kufunafuna mpata woti amuperekere kwa iwo, anthu onse osadziŵa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 Iye anavomera, ndipo anayamba kufunafuna mpata wabwino wakuti amupereke Yesu kwa iwo pamene panalibe gulu la anthu pafupi.

Onani mutuwo Koperani




Luka 22:6
4 Mawu Ofanana  

Koma ananena iwo, pa nthawi ya chikondwerero iai, kuti pasakhale phokoso la anthu.


pakuti anati, Pachikondwerero ai, kuti pangakhale phokoso la anthu.


Ndipo anakondwera, napangana naye kumpatsa ndalama.


Ndipo tsiku la mikate yopanda chotupitsa linafika, limene inayenera kuphedwa nsembe ya Paska.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa