Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 22:5 - Buku Lopatulika

5 Ndipo anakondwera, napangana naye kumpatsa ndalama.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Ndipo anakondwera, napangana naye kumpatsa ndalama.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Iwo adakondwa, nalonjeza kumpatsa ndalama.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Iwo anakondwa ndipo anagwirizana zomupatsa ndalama.

Onani mutuwo Koperani




Luka 22:5
11 Mawu Ofanana  

Ndipo iye anachoka, nalankhulana ndi ansembe aakulu ndi akazembe mompereka Iye kwa iwo.


Ndipo iye anavomera, nafunafuna nthawi yabwino yakumpereka Iye kwa iwo, pakalibe khamu la anthu.


(Uyutu tsono anadzitengera kadziko ndi mphotho ya chosalungama; ndipo anagwa chamutu, naphulika pakati, ndi matumbo ake onse anakhuthuka;


Koma Petro anati kwa iye, Ndalama yako itayike nawe, chifukwa unalingirira kulandira mphatso ya Mulungu ndi ndalama.


posiya njira yolunjika, anasokera, atatsata njira ya Balamu mwana wa Beori, amene anakonda mphotho ya chosalungama;


Ndipo m'chisiriro adzakuyesani malonda ndi mau onyenga; amene chiweruzo chao sichinachedwe ndi kale lomwe, ndipo chitayiko chao sichiodzera.


Tsoka kwa iwo! Pakuti anayenda m'njira ya Kaini, ndipo anadziononga m'chisokero cha Balamu chifukwa cha kulipira, natayika m'chitsutsano cha Kora.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa