Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 22:56 - Buku Lopatulika

56 Ndipo mdzakazi anamuona iye alikukhala m'kuwala kwake kwa moto, nampenyetsa iye, nati, Munthu uyunso anali naye.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

56 Ndipo mdzakazi anamuona iye alikukhala m'kuwala kwake kwa moto, nampenyetsa iye, nati, Munthu uyunso anali naye.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

56 Mtsikana wina wantchito adamuwona atakhala nao pamotopo. Adamuyang'anitsitsa, nati, “Aŵansotu anali naye.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

56 Mtsikana wantchito anamuona atakhala nawo pafupi ndi moto. Iye anamuyangʼanitsitsa ndipo anati, “Munthu uyu anali ndi Yesu.”

Onani mutuwo Koperani




Luka 22:56
8 Mawu Ofanana  

Ndipo Petro adakhala pabwalo: ndipo mdzakazi anadza kwa iye, nanena, Iwenso unali ndi Yesu wa ku Galileya.


Ndipo pofika madzulo anadza Iye pamodzi ndi khumi ndi awiriwo.


Koma Yesu anati, Mlekeni, mumvutiranji? Wandichitira Ine ntchito yabwino.


Pamenepo anaikanso manja m'maso mwake; ndipo anapenyetsa, nachiritsidwa, naona zonse mbee.


Ndipo pamene adasonkha moto m'kati mwa bwalo, nakhala pansi pamodzi, Petro anakhala pakati pao.


Koma anakana, nati, Mkaziwe, sindimdziwa Iye.


Pamenepo mdzakazi wapakhomoyo ananena kwa Petro, Kodi suli iwenso wa ophunzira a munthu uyu? Iyeyu ananena, Sindine.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa