Luka 22:55 - Buku Lopatulika55 Ndipo pamene adasonkha moto m'kati mwa bwalo, nakhala pansi pamodzi, Petro anakhala pakati pao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201455 Ndipo pamene adasonkha moto m'kati mwa bwalo, nakhala pansi pamodzi, Petro anakhala pakati pao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa55 Iwo adasonkha moto m'kati mwa bwalo la nyumbayo, nakhala pansi pamodzi. Petro nayenso adakakhala pakati pao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero55 Koma pamene anasonkha moto pakati pa bwalo la milandu, anakhala onse pansi ndipo Petro anakhalanso pansi. Onani mutuwo |